Chivumbulutso 9:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anapatsa ilo mphamvu si kuti likawaphe, komatu kuti likawazunze miyezi isanu; ndipo mazunzidwe ao anali ngati mazunzidwe a chinkhanira, pamene chiluma munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anapatsa ilo mphamvu si kuti likawaphe, komatu kuti likawazunze miyezi isanu; ndipo mazunzidwe ao anali ngati mazunzidwe a chinkhanira, pamene chiluma munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Silidaloledwe kuŵapha, koma kungoŵazunza pa miyezi isanu. Kuŵaŵa kwake kwa mazunzowo kunkalingana ndi ululu wa chinkhanira chikaluma munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Silinapatsidwe mphamvu yowapha koma yowazunza kwa miyezi isanu. Ndipo ululu umene anthuwo anawumva unali ngati wa chinkhanira chikaluma munthu. Onani mutuwo |