Chivumbulutso 9:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mu utsimo mudatuluka dzombe padziko, ndipo analipatsa ilo mphamvu monga zinkhanira za dziko zili ndi mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo m'utsimo mudatuluka dzombe padziko, ndipo analipatsa ilo mphamvu monga zinkhanira za dziko zili ndi mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Muutsimo mudatuluka dzombe kukaloŵa m'dziko lapansi, ndipo dzombelo lidapatsidwa mphamvu zoluma zonga za zinkhanira za pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndipo mʼkati mwa utsimo munatuluka dzombe kukalowa mʼdziko lapansi ndipo linapatsidwa mphamvu zoluma ngati za zinkhanira pa dziko lapansi. Onani mutuwo |