Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Chivumbulutso 8:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo angelo asanu ndi awiri akukhala nao malipenga anadzikonzera kuti aombe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo angelo asanu ndi awiri akukhala nao malipenga anadzikonzera kuti aombe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono angelo asanu ndi aŵiri amene anali ndi malipenga asanu ndi aŵiri aja adakonzeka kuti alize malipengawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Angelo asanu ndi awiri anakonzekera kuyimba malipenga asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 8:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo tsiku loyamba la mkate wopanda chotupitsa, ophunzira anadza kwa Yesu, nati, Mufuna tikakonzere kuti Paska, kuti mukadye?


Ndipo ndinaona angelo asanu ndi awiri amene amaimirira pamaso pa Mulungu; ndipo anawapatsa malipenga asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa