Chivumbulutso 8:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo utsi wa zofukiza, pamodzi ndi mapemphero a oyera mtima unakwera kutuluka m'dzanja la mngelo, pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo utsi wa zofukiza, pamodzi ndi mapemphero a oyera mtima unakwera kutuluka m'dzanja la mngelo, pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamodzi ndi mapemphero a anthu a Mulunguwo, utsi wa lubaniyo udakwera pamaso pa Mulungu kuchokera m'manja mwa mngelo uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Fungo la lubani pamodzi ndi mapemphero a oyera mtima zinakwera kumwamba kwa Mulungu kuchokera mʼdzanja la mngeloyo. Onani mutuwo |