Chivumbulutso 8:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ndinaona angelo asanu ndi awiri amene amaimirira pamaso pa Mulungu; ndipo anawapatsa malipenga asanu ndi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ndinaona angelo asanu ndi awiri amene amaimirira pamaso pa Mulungu; ndipo anawapatsa malipenga asanu ndi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kenaka ndidaona angelo asanu ndi aŵiri aja amene amaimirira pamaso pa Mulungu, akupatsidwa malipenga asanu ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo ndinaona angelo asanu ndi awiri aja amene amayimirira pamaso pa Mulungu, akupatsidwa malipenga asanu ndi awiri. Onani mutuwo |