Chivumbulutso 8:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo pamene anamasula chizindikiro chachisanu ndi chiwiri, munali chete mu Mwamba monga mwa nthawi ya ora latheka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo pamene anamasula chizindikiro chachisanu ndi chiwiri, munali chete m'Mwamba monga mwa nthawi ya ora latheka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pomaliza Mwanawankhosa uja adamatula chimatiro chachisanu ndi chiŵiri. Pamenepo onse Kumwamba adangoti chete pa hafu la ora. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Atatsekula chomatira chachisanu ndi chiwiri, kumwamba kunakhala chete mphindi makumi atatu. Onani mutuwo |