Chivumbulutso 7:8 - Buku Lopatulika8 Mwa fuko la Zebuloni zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Yosefe zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Benjamini anasindikizidwa chizindikiro zikwi khumi ndi ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mwa fuko la Zebuloni zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Yosefe zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Benjamini anasindikizidwa chizindikiro zikwi khumi ndi ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 A m'fuko la Zebuloni anali zikwi khumi ndi ziŵiri. A m'fuko la Yosefe anali zikwi khumi ndi ziŵiri. A m'fuko la Benjamini anali zikwi khumi ndi ziŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 ochokera fuko la Zebuloni analipo 12,000; ochokera fuko la Yosefe analipo 12,000; ochokera fuko la Benjamini analipo 12,000. Onani mutuwo |