Chivumbulutso 7:5 - Buku Lopatulika5 Mwa fuko la Yuda anasindikizidwa chizindikiro zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Rubeni zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Gadi zikwi khumi ndi ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwa fuko la Yuda anasindikizidwa chizindikiro zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Rubeni zikwi khumi ndi ziwiri. Mwa fuko la Gadi zikwi khumi ndi ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Olembedwa chizindikiro: A m'fuko la Yuda anali zikwi khumi ndi ziŵiri. A m'fuko la Rubeni anali zikwi khumi ndi ziŵiri. A m'fuko la Gadi anali zikwi khumi ndi ziŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ochokera fuko la Yuda analipo 12,000 amene analembedwa chizindikiro. Ochokera fuko la Rubeni analipo 12,000; ochokera fuko la Gadi analipo 12,000; Onani mutuwo |