Chivumbulutso 7:16 - Buku Lopatulika16 sadzamvanso njala, kapena ludzu, kapena silidzawatentha dzuwa, kapena chitungu chilichonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 sadzamvanso njala, kapena ludzu, kapena silidzawatentha dzuwa, kapena chitungu chilichonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Iwo sadzamvanso njala kapena ludzu. Sadzaombedwanso ndi dzuŵa kapena kusauka ndi kutentha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 ‘Iwowa sadzamvanso njala, sadzamvanso ludzu, dzuwa kapena kutentha kulikonse sikudzawawotcha.’ Onani mutuwo |