Chivumbulutso 7:10 - Buku Lopatulika10 ndipo afuula ndi mau aakulu, nanena, Chipulumutso kwa Mulungu wathu wakukhala pa mpando wachifumu, ndi kwa Mwanawankhosa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo afuula ndi mau akulu, nanena, Chipulumutso kwa Mulungu wathu wakukhala pa mpando wachifumu, ndi kwa Mwanawankhosa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ankafuula mokweza mau kuti, “Chipulumutso nchochokera kwa Mulungu wathu wokhala pa mpando wachifumu, ndiponso kwa Mwanawankhosa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo ankafuwula mokweza kuti: “Chipulumutso chimachokera kwa Mulungu wathu, wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa.” Onani mutuwo |