Chivumbulutso 6:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo pamene anamasula chizindikiro chachiwiri, ndinamva chamoyo chachiwiri chikunena, Idza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo pamene anamasula chizindikiro chachiwiri, ndinamva chamoyo chachiwiri nichinena, Idza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kenaka Mwanawankhosa uja adamatula chimatiro chachiŵiri. Ndipo ndidamva Chamoyo chachiŵiri chija chikunena kuti, “Bwera!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mwana Wankhosa atatsekula chomatira chachiwiri, ndinamva chamoyo chachiwiri chija chikuti, “Bwera!” Onani mutuwo |