Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Chivumbulutso 5:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo anadza, nalitenga kudzanja lamanja la Iye wakukhala pa mpando wachifumu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo anadza, nalitenga kudzanja lamanja la Iye wakukhala pa mpando wachifumu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Iyeyo adabwera nkulandira buku lija limene linali m'dzanja lamanja la wokhala pampando wachifumu uja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iye anabwera natenga buku lija limene linali mʼdzanja lamanja la wokhala pa mpando waufumuyo.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 5:7
3 Mawu Ofanana  

Chivumbulutso cha Yesu Khristu, chimene Mulungu anamvumbulutsira achionetsera akapolo ake, ndicho cha izi ziyenera kuchitika posachedwa: ndipo potuma mwa mngelo wake anazindikiritsa izi kwa kapolo wake Yohane;


Ndipo ndinaona m'dzanja lamanja la Iye wakukhala pa mpando wachifumu buku lolembedwa m'kati ndi kunja kwake, losindikizika ndi zizindikiro zisanu ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa