Chivumbulutso 5:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo ndinaona pakati pa mpando wachifumu ndi zamoyo zinai, ndi pakati pa akulu, Mwanawankhosa ali chilili ngati waphedwa; wokhala nazo nyanga zisanu ndi ziwiri, ndi maso asanu ndi awiri, ndiyo mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu, yotumidwa ilowe m'dziko lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo ndinaona pakati pa mpando wachifumu ndi zamoyo zinai, ndi pakati pa akulu, Mwanawankhosa ali chilili ngati waphedwa; wokhala nazo nyanga zisanu ndi ziwiri, ndi maso asanu ndi awiri, ndiyo mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu, yotumidwa ilowe m'dziko lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono ndidaona Mwanawankhosa ataimirira pakati pa mpando wachifumu uja ndi Zamoyo zinai zija ndiponso Akuluakulu 24 aja. Mwanawankhosayo ankaoneka ngati wophedwa, ndipo anali ndi nyanga zisanu ndi ziŵiri ndiponso maso asanu ndi aŵiri. Masowo ndi Mizimu isanu ndi iŵiri ija ya Mulungu yotumidwa m'dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka ndinaona Mwana Wankhosa akuoneka ngati wophedwa atayimirira pakatikati pa mpando waufumu uja ndi zamoyo zinayi zija ndi akuluakulu aja. Mwana Wankhosayo anali ndi nyanga zisanu ndi ziwiri ndi maso asanu ndi awiri omwe ndi Mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu yomwe anayitumiza ku dziko lonse lapansi. Onani mutuwo |