Chivumbulutso 5:5 - Buku Lopatulika5 ndipo mmodzi wa akulu ananena ndi ine, Usalire: taona, Mkango wochokera m'fuko la Yuda, Muzu wa Davide, wapambana kuti akhoza kutsegula buku ndi zizindikiro zake zisanu ndi ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo mmodzi wa akulu ananena ndi ine, Usalire: taona, Mkango wochokera m'fuko la Yuda, Muzu wa Davide, walakika kutsegula buku ndi zizindikiro zake zisanu ndi ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Apo mmodzi mwa Akuluakulu aja adandiwuza kuti, “Usalire, pakuti Mkango wa m'fuko la Yuda, chidzukulu cha mfumu Davide, wapambana, ndipo Iye angathe kufutukula bukulo ndi kumatula zimatiro zake zisanu ndi ziŵiri zija.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsono mmodzi mwa akuluakulu aja anati kwa ine, “Usalire! Taona, Mkango wa fuko la Yuda, Muzu wa Davide, wapambana. Iye angathe kufutukula bukuli ndi kumatula zomatira zisanu ndi ziwirizo.” Onani mutuwo |