Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Chivumbulutso 5:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo ndinalira kwambiri, chifukwa sanapezeke mmodzi woyenera kutsegula bukulo, kapena kulipenya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo ndinalira kwambiri, chifukwa sanapezedwa mmodzi woyenera kutsegula bukulo, kapena kulipenya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Motero ndidalira kwambiri poona kuti sadapezeke woyenera kufutukula bukulo kapena kuyang'anamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndinalira kwambiri chifukwa panalibe amene anapezeka woyenera kufutukula bukuli kapena kuona zamʼkati mwake.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 5:4
4 Mawu Ofanana  

Zitatha izi ndinapenya, ndipo taonani, khomo lotseguka mu Mwamba, ndipo mau oyamba ndinawamva, ngati lipenga lakulankhula ndi ine, anati, Kwera kuno, ndipo ndidzakuonetsa zimene ziyenera kuchitika m'tsogolomo.


Ndipo sanathe mmodzi mu Mwamba, kapena padziko, kapena pansi padziko kutsegula pabukupo, kapena kulipenya.


ndipo mmodzi wa akulu ananena ndi ine, Usalire: taona, Mkango wochokera m'fuko la Yuda, Muzu wa Davide, wapambana kuti akhoza kutsegula buku ndi zizindikiro zake zisanu ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa