Chivumbulutso 5:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ndinaona mngelo wamphamvu wakulalikira ndi mau aakulu, Ayenera ndani kutsegula buku, ndi kumasula zizindikiro zake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ndinaona mngelo wamphamvu wakulalikira ndi mau akulu, Ayenera ndani kutsegula buku, ndi kumasula zizindikiro zake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kenaka ndidaona mngelo wamphamvu akufunsa mokweza mau kuti, “Ndani ali woyenera kufutukula bukuli ndi kumatula zimatiro zake?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo ndinaona mngelo wamphamvu akulengeza ndi mawu okweza kuti, “Ndani ali woyenera kumatula zomatira ndi kufutukula bukuli?” Onani mutuwo |