Chivumbulutso 4:6 - Buku Lopatulika6 ndipo kumpandowo, ngati nyanja yagalasi yonga krustalo; ndipo pakati pa mpandowo, ndi pozinga mpandowo, zamoyo zinai zodzala ndi maso kutsogolo ndi kumbuyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo kumpandowo, ngati nyanja yagalasi yonga krustalo; ndipo pakati pa mpandowo, ndi pozinga mpandowo, zamoyo zinai zodzala ndi maso kutsogolo ndi kumbuyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Patsogolo pake panalinso ngati nyanja yagalasi yonyezimira. Pakatimpakati, pozungulira mpando wachifumu uja, panali Zamoyo zinai, zokhala ndi maso ponseponse, kutsogolo ndi kumbuyo komwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Patsogolo pa mpando waufumu pomwepo panalinso ngati nyanja yagalasi yonyezimira ngati mwala wa krustalo. Pakatinʼpakati, kuzungulira mpando waufumuwo panali zamoyo zinayi zokhala ndi maso ponseponse, kutsogolo ndi kumbuyo komwe. Onani mutuwo |