Chivumbulutso 3:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Filadelfiya lemba: Izi anena Iye amene ali Woyera, Iye amene ali Woona, Iye wakukhala nacho chifungulo cha Davide, Iye wotsegula, ndipo palibe wina atseka; Iye wotseka, ndipo palibe wina atsegula: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Filadelfiya lemba: Izi anena Iye amene ali Woyera, Iye amene ali Woona, Iye wakukhala nacho chifungulo cha Davide, Iye wotsegula, ndipo palibe wina atseka; Iye wotseka, ndipo palibe wina atsegula: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Mtsogoleri wa mpingo wa ku Filadelfiya umlembere kuti, Naŵa mau ochokera kwa Iye amene ali woyera ndi woona, amene ali ndi kiyi yaulamuliro ya Mfumu Davide. Uja amene amati akatsekula, palibe wotinso nkutseka, ndipo akatseka, palibe wotinso nkutsekula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Lembera mngelo wampingo wa ku Filadefiya kuti: Awa ndi mawu ochokera kwa amene ndi woyera ndi woonadi, amene ali ndi kiyi ya Davide. Iye akatsekula palibe amene angatseke; ndipo akatseka palibe amene angatsekule. Onani mutuwo |