Chivumbulutso 3:16 - Buku Lopatulika16 Kotero, popeza uli wofunda, wosati wotentha kapena wozizira, ndidzakulavula m'kamwa mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Kotero, popeza uli wofunda, wosati wotentha kapena wozizira, ndidzakulavula m'kamwa mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma popeza kuti ndinu ofunda chabe, osati otentha kapena ozizira, ndidzakusanzani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsono popeza ndiwe wofunda chabe, sindiwe wotentha kapena wozizira, ndatsala pangʼono kuti ndikulavule mʼkamwa mwanga. Onani mutuwo |