Chivumbulutso 3:11 - Buku Lopatulika11 Ndidza msanga; gwira chimene uli nacho, kuti wina angalande korona wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndidza msanga; gwira chimene uli nacho, kuti wina angalande korona wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndikubwera posachedwa. Gwiritsani chimene muli nacho, kuti wina angakulandeni mphotho yanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ine ndikubwera msanga. Gwiritsitsa chimene uli nacho kuti wina angakulande chipewa chako chaufumu. Onani mutuwo |