Chivumbulutso 22:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ananena kwa ine, Tapenya, usachite; ndine kapolo mnzako, ndi mnzao wa abale ako aneneri, ndi wa iwo akusunga mau a buku ili; lambira Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ananena kwa ine, Tapenya, usachite; ndine kapolo mnzako, ndi mnzao wa abale ako aneneri, ndi wa iwo akusunga mau a buku ili; lambira Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 koma iye adandiwuza kuti, “Zimenezo iyai. Ndine mtumiki chabe, ngati iwe wemwe, ngati abale ako aneneri, ndiponso ngati onse otsata mau olembedwa m'buku lino. Iwe pembedza Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma mngeloyo anandiwuza kuti, “Usatero ayi! Ine ndine wotumikira monga iwe pamodzi ndi abale ako aneneri ndi onse amene amasunga mawu a mʼbuku pembedzani Mulungu.” Onani mutuwo |