Chivumbulutso 22:4 - Buku Lopatulika4 nadzaona nkhope yake; ndipo dzina lake lidzakhala pamphumi pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 nadzaona nkhope yake; ndipo dzina lake lidzakhala pamphumi pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iwo azidzaona nkhope yake, ndipo dzina lake lidzakhala lolembedwa pamphumi pao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iwo adzaona nkhope yake ndipo dzina lake lidzalembedwa pa mphumi zawo. Onani mutuwo |