Chivumbulutso 20:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anagwira chinjoka, njoka yakaleyo, ndiye mdierekezi ndi Satana, nammanga iye zaka chikwi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anagwira chinjoka, njoka yakaleyo, ndiye mdierekezi ndi Satana, nammanga iye zaka chikwi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adagwira Chinjoka chija, ndiye kuti njoka yakale ija yotchedwa Mdyerekezi ndiponso Satana, nachimanga zaka chikwi chimodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anachigwira chinjokacho, chinjoka chakalekale chija, amene ndi Mdierekezi kapena kuti Satana, ndipo anamumanga zaka 1,000. Onani mutuwo |