Chivumbulutso 2:6 - Buku Lopatulika6 Koma ichi uli nacho, kuti udana nazo ntchito za Anikolai, zimene Inenso ndidana nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma ichi uli nacho, kuti udana nazo ntchito za Anikolai, zimene Inenso ndidana nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Komabe chokomera chanu ndi ichi chakuti, mumadana ndi zochita za Anikolai, zimene inenso ndimadana nazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Komabe chokomera chako ndi chakuti umadana ndi zochita za Anikolai, zimene Inenso ndimadana nazo. Onani mutuwo |