Chivumbulutso 2:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Pergamo lemba: Izi anena Iye wokhala nalo lupanga lakuthwa konsekonse: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Pergamo lemba: Izi anena Iye wokhala nalo lupanga lakuthwa konsekonse: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Mtsogoleri wa mpingo wa ku Pergamo umlembere kuti: Naŵa mau ochokera kwa uja ali ndi lupanga lakuthwa konsekonse lija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Lembera mngelo wa mpingo wa ku Pergamo kuti: Awa ndi mawu ochokera kwa amene ali ndi lupanga lakuthwa konsekonse. Onani mutuwo |