Chivumbulutso 19:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anagwa pansi akuluwo makumi awiri mphambu anai ndi zamoyo zinai, ndipo zinalambira Mulungu wakukhala pa mpando wachifumu, ndi kunena, Amen; Aleluya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anagwa pansi akuluwo makumi awiri mphambu anai ndi zamoyo zinai, ndipo zinalambira Mulungu wakukhala pa mpando wachifumu, nizinena, Amen; Aleluya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Akuluakulu 24 aja, pamodzi ndi Zamoyo zinai zija, adadzigwetsa pansi moŵerama, napembedza Mulungu amene amakhala pa mpando wachifumu. Adayankha kuti, “Amen, Aleluya!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Akuluakulu 24 aja ndi zamoyo zinayi zija anadzigwetsa pansi kupembedza Mulungu amene anakhala pa mpando waufumu. Ndipo anafuwula kuti, “Ameni, Haleluya!” Onani mutuwo |