Chivumbulutso 19:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anatinso, Aleluya. Ndipo utsi wake ukwera kunthawi za nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anatinso, Aleluya. Ndipo utsi wake ukwera kunthawi za nthawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kachiŵiri mau aja adanenanso kuti, “Aleluya! Utsi wa mzindawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” Onani mutuwo |