Chivumbulutso 18:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ochita malonda a m'dziko adzalira nadzauchitira chifundo, popeza palibe munthu agulanso malonda ao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ochita malonda a m'dziko adzalira nadzauchitira chifundo, popeza palibe munthu agulanso malonda ao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu amalonda a pa dziko lapansi adzalira ndi kumva naye chisoni kwambiri, pakuti palibenso wogula malonda ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Amalonda a dziko lapansi adzalira nakhuza maliro ake chifukwa palibenso amene akugula katundu wawo, Onani mutuwo |