Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Chivumbulutso 13:9 - Buku Lopatulika

9 Ngati wina ali nalo khutu, amve.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ngati wina ali nalo khutu, amve.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ngati wina ali ndi makutu, amve.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iye amene ali ndi makutu, amve.

Onani mutuwo Koperani




Chivumbulutso 13:9
7 Mawu Ofanana  

Amene ali ndi makutu akumva, amve.


Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.


Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena Iye izi anafuula, Iye amene ali ndi makutu akumva amve.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Iye amene apambana sadzachitidwa choipa ndi imfa yachiwiri.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye amene apambana ndidzampatsa kudya za ku mtengo wa moyo umene uli mu Paradaiso wa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa