Chivumbulutso 13:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo chilombo ndinachionacho chinafanana ndi nyalugwe, ndi mapazi ake ngati mapazi a chimbalangondo, ndi pakamwa pake ngati pakamwa pa mkango; ndipo chinjoka chinampatsa iye mphamvu yake, ndi mpando wachifumu wake, ndi ulamuliro waukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo chilombo ndinachionacho chinafanana ndi nyalugwe, ndi mapazi ake ngati mapazi a chimbalangondo, ndi pakamwa pake ngati pakamwa pa mkango; ndipo chinjoka chinampatsa iye mphamvu yake, ndi mpando wachifumu wake, ndi ulamuliro waukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chilombo chimene ndidaaonacho chinali ngati kambuku, mapazi ake ngati a chimbalangondo, kukamwa kwake ngati kwa mkango. Chinjoka chija chidaapatsa chilombocho mphamvu zake, mpando wake wachifumu, ndiponso ulamuliro waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Chirombo chimene ndinachionacho chinali ngati kambuku, mapazi ake ngati chimbalangondo, kukamwa kwake ngati kwa mkango. Chinjoka chija chinapatsa chirombocho mphamvu zake, mpando wake waufumu ndiponso ulamuliro waukulu. Onani mutuwo |