Chivumbulutso 12:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo chinaoneka chizindikiro china m'mwamba taonani, chinjoka chofiira, chachikulu, chakukhala nayo mitu isanu ndi iwiri, ndi nyanga khumi, ndi pamutu pake nduwira zachifumu zisanu ndi ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo chinaoneka chizindikiro china m'mwamba taonani, chinjoka chofiira, chachikulu, chakukhala nayo mitu isanu ndi iwiri, ndi nyanga khumi, ndi pamutu pake nduwira zachifumu zisanu ndi ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kudaonekanso chizindikiro china kuthambo: chinjoka chachikulu, chofiira, cha mitu isanu ndi iŵiri ndi nyanga khumi; pa mutu uliwonse chitavala chisoti chaufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka ku thambo kunaonekanso chizindikiro china; chinjoka chachikulu kwambiri, chofiira chomwe chinali ndi mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi; pamutu uliwonse chitavala chipewa chaufumu. Onani mutuwo |