Chivumbulutso 12:2 - Buku Lopatulika2 ndipo anali ndi pakati; ndipo afuula alimkubala, ndi kumva zowawa zakubala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndipo anali ndi pakati; ndipo afuula alimkubala, ndi kumva zowawa zakubala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Maiyo anali ndi pathupi, ndipo pa nthaŵi yochira adalira nako mokuwa kupweteka kwa kubala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mayiyo anali woyembekezera ndipo pa nthawi yake yochira analira mokuwa chifukwa cha ululu wakubala. Onani mutuwo |