Chivumbulutso 11:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo bwalo la kunja kwa Kachisi ulisiye padera, osaliyesa; pakuti adapatsa ilo kwa amitundu; ndipo mzinda wopatulika adzaupondereza miyezi makumi anai mphambu iwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo bwalo la kunja kwa Kachisi ulisiye padera, osaliyesa; pakuti adapatsa ilo kwa amitundu; ndipo mzinda wopatulika adzaupondereza miyezi makumi anai mphambu iwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Koma bwalo la kunja kwa Nyumbayo ulisiye, osaliyesa. Bwalo limeneli lidapatsidwa kwa anthu akunja, ndipo iwowo adzaupondereza Mzinda woyerawo pa miyezi 42. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma bwalo lakunja ulisiye, usaliyeze chifukwa linaperekedwa kwa a mitundu ina. Iwo adzawupondereza mzinda woyerawo kwa miyezi 42. Onani mutuwo |