Chivumbulutso 11:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anamva mau aakulu akuchokera Kumwamba akunena nao, Kwerani kuno. Ndipo anakwera kunka Kumwamba mumtambo; ndipo adani ao anawapenya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anamva mau akulu akuchokera Kumwamba akunena nao, Kwerani kuno. Ndipo anakwera kunka Kumwamba mumtambo; ndipo adani ao anawapenya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Aneneri aja adamva mau amphamvu ochokera Kumwamba oŵauza kuti, “Bwerani kuno.” Iwowo adapitadi Kumwamba mu mtambo, adani ao aja akuŵapenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kenaka aneneri aja anamva mawu ofuwula ochokera kumwamba owawuza kuti, “Bwerani kuno.” Ndipo anapitadi kumwamba mu mtambo adani awo aja akuwaona. Onani mutuwo |