Chivumbulutso 11:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo anandipatsa ine bango ngati ndodo, ndi kuti, Tanyamuka, nuyese Kachisi wa Mulungu, ndi guwa la nsembe, ndi iwo akulambiramo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo anandipatsa ine bango ngati ndodo, ndi kuti, Tanyamuka, nuyese Kachisi wa Mulungu, ndi guwa la nsembe, ndi iwo akulambiramo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pambuyo pake adandipatsa bango loyesera, longa ndodo, nandiwuza kuti, “Nyamuka, kayese Nyumba ya Mulungu ndi guwa lansembe, ndipo ukaŵerenge opembedza m'Nyumbamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndinapatsidwa bango longa ndodo yoyezera ndipo ndinawuzidwa kuti, “Pita, kayeze Nyumba ya Mulungu ndi guwa lansembe, ndipo ukawerenge anthu opembedza mʼNyumbamo. Onani mutuwo |