Chivumbulutso 10:7 - Buku Lopatulika7 komatu m'masiku a mau a mngelo wachisanu ndi chiwiri m'mene iye adzayamba kuomba lipenga, pamenepo padzatsirizika chinsinsi cha Mulungu, monga analalikira kwa akapolo ake aneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 komatu m'masiku a mau a mngelo wachisanu ndi chiwiri m'mene iye adzayamba kuomba lipenga, pamenepo padzatsirizika chinsinsi cha Mulungu, monga analalikira kwa akapolo ake aneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pamene mngelo wachisanu ndi chiŵiri adzaliza lipenga lake, zachinsinsi zimene Mulungu adakonzeratu zidzachitika, monga momwe Iye adaalonjezera kwa atumiki ake aja, aneneri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma patsala pangʼono kuti mngelo wachisanu ndi chiwiri uja awombe lipenga lake, chinsinsi cha Mulungu chidzachitika monga momwe analengezera kwa atumiki ake, aneneri.” Onani mutuwo |