Chivumbulutso 10:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo mngelo amene ndinamuona alikuimirira panyanja ndi pa mtunda, anakweza dzanja lake lamanja kuloza kumwamba, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo mngelo amene ndinamuona alikuimirira panyanja ndi pa mtunda, anakweza dzanja lake lamanja kuloza kumwamba, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamenepo mngelo amene ndidaaona ataponda pa nyanja ndi pa mtunda uja, adakweza dzanja lake lamanja kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kenaka mngelo amene ndinamuona ataponda mʼnyanja ndi ku mtunda uja, anakweza dzanja lake lamanja kumwamba. Onani mutuwo |