Chivumbulutso 10:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ananena nane, Uyenera iwe kuneneranso pa anthu ndi mitundu, ndi manenedwe, ndi mafumu ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ananena nane, Uyenera iwe kuneneranso pa anthu ndi mitundu, ndi manenedwe, ndi mafumu ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pamenepo adandiwuza kuti, “Uyenera kulengezanso za mitundu yambiri ya anthu, za zilankhulo zosiyanasiyana, ndi za mafumu ambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo anandiwuza kuti, “Iwe uyenera kulalikiranso za mitundu yambiri ya anthu, za mayiko, ziyankhulo ndi za mafumu.” Onani mutuwo |