Chivumbulutso 1:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo m'dzanja lake lamanja munali nyenyezi zisanu ndi ziwiri; ndi m'kamwa mwake mudatuluka lupanga lakuthwa konsekonse; ndipo nkhope yake ngati dzuwa lowala mu mphamvu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo m'dzanja lake lamanja munali nyenyezi zisanu ndi ziwiri; ndi m'kamwa mwake mudatuluka lupanga lakuthwa konsekonse; ndipo nkhope yake ngati dzuwa lowala mu mphamvu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 M'dzanja lake lamanja adaanyamula nyenyezi zisanu ndi ziŵiri, ndipo m'kamwa mwake munali lupanga lakuthwa konsekonse lotulukira kunja. Nkhope yake inali yoŵala ngati dzuŵa lamasana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Mʼdzanja lake lamanja ananyamula nyenyezi zisanu ndi ziwiri, ndipo mʼkamwa mwake munali lupanga lakuthwa konsekonse. Nkhope yake imawala ngati dzuwa lowala kwambiri. Onani mutuwo |