Chivumbulutso 1:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo ndinacheuka kuona wonena mau amene adalankhula ndi ine. Ndipo nditacheuka ndinaona zoikaponyali zisanu ndi ziwiri zagolide; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo ndinacheuka kuona wonena mau amene adalankhula ndi ine. Ndipo nditacheuka ndinaona zoikapo nyali zisanu ndi ziwiri zagolide; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nditacheuka kuti ndiwone akundilankhula ndani, ndidaona ndodo zoikapo nyale zisanu ndi ziŵiri zagolide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Nditatembenuka kuti ndione amene amandiyankhulayo, ndinaona zoyikapo nyale zisanu ndi ziwiri zagolide. Onani mutuwo |