Chivumbulutso 1:11 - Buku Lopatulika11 ndi kuti, Chimene upenya, lemba m'buku, nulitumize kwa Mipingo isanu ndi iwiri, ku Efeso, ndi ku Smirina, ndi ku Pergamo, ndi ku Tiatira, ndi ku Sardi, ndi ku Filadelfiya, ndi ku Laodikea. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 ndi kuti, Chimene upenya, lemba m'buku, nulitumize kwa Mipingo isanu ndi iwiri, ku Efeso, ndi ku Smirina, ndi ku Pergamo, ndi ku Tiatira, ndi ku Sardi, ndi ku Filadelfiya, ndi ku Laodikea. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Liwulo lidati, “Zimene ukuwonazi, uzilembe m'buku ndipo ulitumize kwa mipingo isanu ndi iŵiri iyi: wa ku Efeso, wa ku Smirina, wa ku Pergamo, wa ku Tiatira, wa ku Sardi, wa ku Filadelfiya ndi wa ku Laodikea.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 amene anati, “Lemba mʼbuku zimene ukuziona ndipo uzitumize ku mipingo isanu ndi iwiri ya ku Efeso, Simurna, Pergamo, Tiyatira, Sarde, Filadefiya ndi ku Laodikaya.” Onani mutuwo |