Amosi 9:12 - Buku Lopatulika12 kuti alandire otsala a Edomu akhale cholowa chao, ndi amitundu onse a kutchedwa dzina langa, ati Yehova wakuchita izi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 kuti alandire otsala a Edomu akhale cholowa chao, ndi amitundu onse a kutchedwa dzina langa, ati Yehova wakuchita izi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nthaŵi imeneyo Aisraele otsala adzagonjetsa zimene zatsala za ku Edomu, pamodzi ndi maiko onse amene amadziŵika ndi dzina langa.” Akuterotu Chauta, amene adzachitedi zimene wanenazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 kuti adzatengenso otsala a Edomu ndi mitundu yonse imene imatchedwa ndi dzina langa,” akutero Yehova amene adzachita zinthu izi. Onani mutuwo |