Amosi 9:11 - Buku Lopatulika11 Tsiku lomwelo ndidzautsa msasa wa Davide udagwawo, ndi kukonzanso zopasuka zake; ndipo ndidzautsa zogumuka zake, ndi kuumanga monga masiku a kalelo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Tsiku lomwelo ndidzautsa msasa wa Davide udagwawo, ndi kukonzanso zopasuka zake; ndipo ndidzautsa zogumuka zake, ndi kuumanga monga masiku a kalelo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta akuti, “Nthaŵi imeneyo ndidzakwezanso ufumu wa Davide umene udagwa ngati nyumba. Ndidzakonzanso makoma ake ogumuka ndi kumanganso mabwinja ake. Ndidzaubwezeranso mwake mwakale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Tsiku limenelo ndidzabwezeretsa nyumba ya Davide imene inagwa. Ndidzakonzanso malo amene anagumuka, ndi kuyimanganso monga inalili poyamba, Onani mutuwo |
Dziko lonse lidzasandulika, lidzanga chidikha, kuyambira ku Geba kufikira ku Rimoni, kumwera kwa Yerusalemu; ndipo pali uwupo padzakhala ponyamuka, ndipo udzakhala m'malo mwake, kuyambira ku Chipata cha Benjamini kufikira ku malo a chipata choyamba, kufikira ku Chipata cha Kungodya, ndi kuyambira Nsanja ya Hananele kufikira ku zoponderamo mphesa za mfumu.