Amosi 8:14 - Buku Lopatulika14 Iwo akulumbira ndi kutchula tchimo la Samariya, ndi kuti, Pali Mulungu wako, Dani; ndipo, Pali moyo wa njira ya ku Beereseba, iwowa adzagwa, osaukanso konse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Iwo akulumbira ndi kutchula tchimo la Samariya, ndi kuti, Pali Mulungu wako, Dani; ndipo, Pali moyo wa njira ya ku Beereseba, iwowa adzagwa, osaukanso konse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Onse amene amalumbira m'dzina la Asima, mulungu wa Samariya, nkumanena kuti, ‘Pali mulungu wa ku Dani!’ Kapena kuti, ‘Pali njira yopatulika ya ku Beereseba!’ Onsewo adzagwa osadzukanso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Onse amene amalumbira pa tchimo la Samariya, kapena kumanena kuti, ‘Iwe Dani, pali mulungu wako wamoyo,’ kapena, ‘Pali mulungu wamoyo wa ku Beeriseba.’ Iwowo adzagwa ndipo sadzadzukanso.” Onani mutuwo |