Amosi 6:13 - Buku Lopatulika13 inu okondwera nacho chopanda pake, ndi kuti, Kodi sitinadzilimbitse tokha ndi kulanda Karinaimu mwa mphamvu yathuyathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 inu okondwera nacho chopanda pake, ndi kuti, Kodi sitinadzilimbitsa tokha ndi kulanda Karinaimu mwa mphamvu yathuyathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mukunyadira kuti mudagonjetsa mzinda wa Lodebara, mukunena kuti, “Kodi suja tidapambana mzinda wa Karinaimu ndi mphamvu zathu zokha?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Inu amene mukunyadira kuti munagonjetsa Lo Debara ndipo mukunena kuti, “Kodi sitinatenge Karinaimu ndi mphamvu zathu zokha?” Onani mutuwo |