Amosi 6:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti taonani, Yehova walamulira, nadzakantha nyumba yaikulu ichite mpata, ndi nyumba yaing'ono ichite mindala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti taonani, Yehova walamulira, nadzakantha nyumba yaikulu ichite mpata, ndi nyumba yaing'ono ichite mindala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Zoonadi, Chauta akadzangolamula, nyumba zikuluzikulu zidzagamukagamuka, ndipo nyumba zing'onozing'ono ndiye zidzangosanduka zibuma zokhazokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pakuti Yehova walamula kuti nyumba zikuluzikulu Iye adzazigamulagamula, ndipo nyumba zazingʼono zidzasanduka maduka okhaokha. Onani mutuwo |