Amosi 5:27 - Buku Lopatulika27 M'mwemo ndidzakutengani kunka nanu kundende kutsogolo kwa Damasiko, ati Yehova, amene dzina lake ndiye Mulungu wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 M'mwemo ndidzakutengani kunka nanu kundende kutsogolo kwa Damasiko, ati Yehova, amene dzina lake ndiye Mulungu wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Pakuti ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira mzinda wa Damasiko.” Akutero Chauta, amene dzina lake ndi Mulungu Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,” akutero Yehova, amene dzina lake ndi Mulungu Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |