Amosi 5:26 - Buku Lopatulika26 Inde mwasenza hema wa mfumu yanu, ndi tsinde la mafano anu, nyenyezi ya mulungu wanu, amene mudadzipangira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Inde mwasenza hema wa mfumu yanu, ndi tsinde la mafano anu, nyenyezi ya mulungu wanu, amene mudadzipangira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndipotu muzidzanyamula Sakuti, mfumu yanu, ndi nyenyezi ija Kaiwani, mulungu wanu, mafano amene mudadzipangira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu, ndi nyenyezi ija Kaiwani, mulungu wanu, mafano amene munadzipangira. Onani mutuwo |