Amosi 5:25 - Buku Lopatulika25 Ngati munabwera nazo kwa Ine nsembe zophera ndi zaufa zaka makumi anai m'chipululu, inu nyumba ya Israele? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ngati munabwera nazo kwa Ine nsembe zophera ndi zaufa zaka makumi anai m'chipululu, inu nyumba ya Israele? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 “Kodi inu anthu a ku Israele, zaka makumi anai zimene mudakhala m'chipululu, mudanditsirirako nsembe ndi kundipatsa mitulo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 “Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja munkandibweretsera nsembe ndi zopereka, inu nyumba ya Israeli? Onani mutuwo |