Amosi 5:24 - Buku Lopatulika24 Koma chiweruzo chiyende ngati madzi, ndi chilungamo ngati mtsinje wosefuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma chiweruzo chiyende ngati madzi, ndi chilungamo ngati mtsinje wosefuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma kuweruza kwanu kwangwiro kuziyenda kosalekeza ngati madzi, kulungama kwanu kukhale ngati mtsinje wosaphwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi, chilungamo ngati mtsinje wosaphwa! Onani mutuwo |